-
Oweruza 3:28Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
28 Kenako anawauza kuti: “Nditsatireni, chifukwa Yehova wapereka adani anu Amowabu mʼmanja mwanu.” Atatero, anamʼtsatira kukatsekereza Amowabu pamalo owolokera mtsinje wa Yorodano, ndipo sanalole aliyense kuwoloka.
-