Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 7:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Akhate aja atafika mʼmbali mwa msasawo, analowa mutenti ina ndipo anayamba kudya ndi kumwa. Kenako anatengamo siliva, golide ndi zovala nʼkupita kukazibisa. Atatero anabwerera nʼkudzalowanso mutenti ina ndipo anatengamonso zinthu zina nʼkukazibisa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena