Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 7:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndiyeno mtumiki wina wa mfumu anati: “Uzani anthu atenge mahatchi 5 pa mahatchi amene atsala mumzindawu ndipo muwatume akaone. Zimene zingakawachitikire anthuwo sizingasiyane ndi zimene zichitikire gulu la Aisiraeli amene atsala mumzindamu. Komanso sizingasiyane ndi zimene zachitikira gulu la Aisiraeli amene afa.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena