-
2 Mafumu 8:9Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
9 Choncho Hazaeli anatenga mphatso nʼkupita kukakumana naye. Mphatsozo anazinyamula pa ngamira zokwana 40. Anatenga chinthu chilichonse chabwino cha ku Damasiko. Atafika kwa Elisa anamuuza kuti: “Mwana wanu Beni-hadadi mfumu ya Siriya wandituma kudzakufunsani kuti, ‘Kodi ndichira matenda angawa?’”
-