Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 10:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Yehu atachoka pamenepo, anakumana ndi Yehonadabu+ mwana wa Rekabu+ amene anabwera kudzakumana naye. Atamupatsa moni,* anamʼfunsa kuti: “Kodi mtima wako wonse uli ndi ine ngati mmene mtima wanga ulili ndi mtima wako?”

      Yehonadabu anayankha kuti: “Inde.”

      Ndiyeno Yehu anati: “Ngati ndi choncho ndipatse dzanja lako.”

      Choncho Yehonadabu anapereka dzanja lake ndipo Yehu anamukweza mʼgaleta lake.

  • 2 Mafumu
    Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019
    • 10:15

      Nsanja ya Olonda,

      8/1/2005, tsa. 11

      1/1/1998, ptsa. 12-13

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena