Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 24:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Kenako Semaya mwana wa Netaneli mlembi wa Alevi, anawalemba mayina pamaso pa mfumu, akalonga, wansembe Zadoki,+ Ahimeleki+ mwana wa Abiyatara+ ndiponso pamaso pa atsogoleri a nyumba za makolo za ansembe ndi za Alevi. Ankasankha nyumba imodzi ya makolo kuchokera kwa ana a Eleazara kenako nʼkusankhanso nyumba imodzi ya makolo kuchokera kwa ana a Itamara.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena