Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 35:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Choncho Neko anatumiza anthu kuti akamuuze kuti: “Kodi chikukukhudza nʼchiyani iwe mfumu ya Yuda? Ulendo uno sindinabwere kudzamenyana ndi iwe. Ndabwera kudzamenyana ndi mtundu wina ndipo Mulungu wanena kuti ndisachedwe. Ngati ukufuna kuti zinthu zikuyendere bwino, usachite zimenezi. Usatsutsane ndi Mulungu amene ali ndi ine chifukwa akhoza kukuwononga.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena