-
Nehemiya 8:11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 Alevi ankauza anthu onse kuti asachite phokoso. Ankanena kuti: “Khalani chete chifukwa lero ndi tsiku lopatulika, choncho musadzimvere chisoni.”
-