4 Ku Yerusalemu kunkakhalanso anthu ena a fuko la Yuda ndi la Benjamini.) Anthu a fuko la Yudawo anali Ataya mwana wa Uziya. Uziyayo anali mwana wa Zekariya, Zekariya anali mwana wa Amariya, Amariya anali mwana wa Sefatiya, Sefatiya anali mwana wa Mahalalele wochokera mʼbanja la Perezi.+