22 Woyangʼanira Alevi ku Yerusalemu anali Uzi mwana wa Bani. Bani anali mwana wa Hasabiya, Hasabiya anali mwana wa Mataniya,+ Mataniya anali mwana wa Mika wa mʼbanja la Asafu ndipo a mʼbanja la Asafu anali oimba. Uzi ankayangʼanira ntchito yapanyumba ya Mulungu woona