-
Nehemiya 12:27Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
27 Ndiyeno mwambo wotsegulira mpanda wa Yerusalemu uli pafupi, anthu anafunafuna Alevi mʼmadera onse amene ankakhala nʼkubwera nawo ku Yerusalemu. Anachita izi kuti potsegulira mpandawo pakhale kusangalala, kuimba nyimbo zoyamika Mulungu+ ndiponso kuimba pogwiritsa ntchito zinganga, zoimbira za zingwe ndi azeze.
-