-
Nehemiya 12:44Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
44 Pa tsikuli anasankha amuna kuti aziyangʼanira nyumba zosungiramo+ zopereka,+ mbewu zoyambirira kucha+ ndiponso chakhumi.+ Anawapatsa udindo woti azitutira mʼnyumbamo magawo oyenera kuperekedwa kwa ansembe ndi Alevi+ mogwirizana ndi Chilamulo,+ kuchokera mʼminda yonse yamʼmizinda yawo. Popeza anthu a ku Yuda anasangalala chifukwa cha ansembe ndi Alevi amene ankatumikira.
-