-
Yobu 10:17Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
17 Mumabweretsa mboni zatsopano kuti zinditsutse
Ndipo mumawonjezera mkwiyo wanu pa ine,
Moti mavuto anga akungotsatizanatsatizana.
-