Salimo 45:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Ndidzachititsa kuti anthu adziwe dzina lanu mʼmibadwo yonse yamʼtsogolo.+ Nʼchifukwa chake mitundu ya anthu idzakutamandani mpaka kalekale. Masalimo Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 45:17 Nsanja ya Olonda,2/15/2014, tsa. 12
17 Ndidzachititsa kuti anthu adziwe dzina lanu mʼmibadwo yonse yamʼtsogolo.+ Nʼchifukwa chake mitundu ya anthu idzakutamandani mpaka kalekale.