-
Yesaya 7:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Ndiyeno kunyumba ya Davide kunapita uthenga wakuti: “Dziko la Siriya lachita mgwirizano ndi dziko la Efuraimu.”
Choncho mtima wa Ahazi ndi wa anthu ake unayamba kunjenjemera, ngati mitengo ya mʼnkhalango imene ikugwedezeka ndi mphepo.
-