-
Yesaya 9:17Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
17 Nʼchifukwa chake Yehova sadzasangalala ndi anyamata awo,
Ndipo sadzamvera chisoni ana awo amasiye ndi akazi awo amasiye,
Chifukwa onsewo ndi ampatuko komanso ochita zoipa+
Ndipo pakamwa paliponse pakulankhula zopanda nzeru.
Chifukwa cha zonsezi, mkwiyo wake sunabwerere,
Koma dzanja lake lidakali lotambasula kuti awalange.+
-