Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 18:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Onsewo adzasiyidwa kuti adyedwe ndi mbalame zamʼmapiri zodya nyama

      Komanso nyama zakutchire zapadziko lapansi.

      Mbalame zodya nyamazo zidzakhala zikuwadya nyengo yonse yachilimwe,

      Ndipo nyama zonse zakutchire za padziko lapansi zidzakhala zikuwadya nthawi yonse yokolola.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena