-
Yesaya 28:20Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
20 Chifukwa bedi lafupika kwambiri moti munthu sangathe kugonapo mowongoka bwinobwino,
Ndipo chofunda chachepa kwambiri moti sichikukwanira bwinobwino kuti munthu afunde.
-