7 Kenako gulu la mitundu yonse imene ikuchita nkhondo ndi Ariyeli,+
Onse amene akumenyana naye,
Amene akumumangira nsanja zomenyerapo nkhondo kuti amenyane naye
Ndiponso amene akumubweretsera mavuto,
Adzaona ngati akulota, ngati akuona masomphenya a usiku.