2 Amandifunafuna tsiku lililonse,
Ndipo amasonyeza kuti akusangalala kudziwa njira zanga,
Ngati kuti unali mtundu umene unkachita zinthu zolungama
Ndiponso sunasiye chilungamo cha Mulungu wawo.+
Iwo akundipempha chiweruzo cholungama,
Ngati kuti akufunitsitsa kuyandikira kwa Mulungu.+ Akunena kuti: