-
Yeremiya 26:15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 Koma mudziwe kuti mukandipha, inuyo, mzindawu ndi anthu onse amene akukhala mumzindawu mukhala ndi mlandu wa magazi chifukwa chopha munthu wosalakwa. Ndithudi, Yehova ndi amene wandituma kuti ndidzakuuzeni mawu onse amene mwamvawa.”
-