-
Yeremiya 27:4Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
4 Ukatero, uwalamule kuti akauze ambuye awo kuti:
“Mukauze ambuye anu kuti Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, Mulungu wa Isiraeli, wanena kuti,
-