-
Yeremiya 40:5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
5 Yeremiya akuganizira koti apite, Nebuzaradani anamuuza kuti: “Bwerera kwa Gedaliya,+ mwana wa Ahikamu,+ mwana wa Safani,+ amene mfumu ya Babulo yamuika kuti azilamulira mizinda ya Yuda. Ukakhale naye pakati pa anthuwo, kapena ukhoza kupita kulikonse kumene ungakonde.”
Kenako mkulu wa asilikali olondera mfumu anamupatsa chakudya chapaulendo ndi mphatso ndipo anamulola kuti apite.
-