Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 12:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Anthu amʼdzikoli uwauze kuti, ‘Izi nʼzimene Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kwa anthu amene akukhala mu Yerusalemu, mʼdziko la Isiraeli: “Iwo adzadya chakudya chawo ali ndi nkhawa ndipo adzamwa madzi ali ndi mantha aakulu. Izi zidzachitika chifukwa dziko lawo lidzakhala bwinja lokhalokha+ chifukwa cha zinthu zachiwawa zimene anthu onse amene akukhala mmenemo akuchita.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena