Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 16:52
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 52 Tsopano iweyo ukuyenera kuchita manyazi chifukwa waikira kumbuyo makhalidwe a azichemwali ako. Iwowo ndi olungama kuposa iweyo chifukwa cha tchimo lako lochita zinthu zonyansa kwambiri kuposa zimene iwowo anachita. Choncho uchite manyazi ndi kunyozeka chifukwa chakuti wachititsa kuti azichemwali ako aoneke ngati olungama.’

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena