-
Ezekieli 31:18Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
18 ‘Kodi ndi mtengo uti pakati pa mitengo ya mu Edeni umene unkafanana ndi iwe pa nkhani ya ulemerero ndi kukula?+ Koma ndithu udzafa* limodzi ndi mitengo ya mu Edeni. Udzagona pakati pa anthu osadulidwa limodzi ndi ophedwa ndi lupanga. Mtengo umenewu ukuimira Farao ndi magulu onse a anthu amene amamutsatira,’ akutero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.”
-