-
Ezekieli 32:14Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
14 Pa nthawi imeneyo ndidzayeretsa madzi awo,
Ndipo ndidzachititsa kuti madzi amʼmitsinje yawo ayende ngati mafuta,’ akutero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.
-