Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 39:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 ‘Pa tsiku limenelo Gogi+ ndidzamupatsa malo kuti akhale manda ake ku Isiraeli komweko, mʼchigwa chimene anthu amene amapita kumʼmawa kwa nyanja amadutsa, ndipo chigwacho chidzatseka njira imene anthu amadutsa. Kumeneko nʼkumene adzaike mʼmanda Gogi limodzi ndi magulu onse a anthu amene ankamutsatira ndipo adzalitchula kuti Chigwa cha Hamoni-Gogi.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena