-
Ezekieli 40:32Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
32 Atandilowetsa mʼbwalo lamkati kudzera kumʼmawa, anayeza kanyumba kapagetiko ndipo anapeza kuti miyezo yake ndi yofanana ndi ya tinyumba tina tija.
-