-
Ezekieli 40:37Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
37 Zipilala zake zamʼmbali zinayangʼana kubwalo lakunja ndipo pazipilala zonsezo panali zithunzi za mtengo wa kanjedza. Anthu akafuna kulowa mʼkanyumbako amakwera masitepe 8.
-