Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 46:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ngati mtsogoleri wa anthu akupereka kwa ansembe nsembe yopsereza yathunthu+ kapena nsembe zamgwirizano kuti zikhale nsembe yaufulu yoperekedwa kwa Yehova, azimutsegulira geti lakumʼmawa. Mtsogoleriyo azipereka kwa ansembe nsembe yake yopsereza yathunthu ndi nsembe zake zamgwirizano ngati mmene amachitira pa tsiku la Sabata.+ Akatuluka getilo lizitsekedwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena