Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 11:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Iye adzasonkhanitsa mphamvu zake ndi kulimbitsa mtima wake kuti aukire mfumu yakumʼmwera ali ndi gulu lalikulu la asilikali. Mfumu yakumʼmwera nayonso idzakonzekera nkhondo ndipo idzasonkhanitsa gulu la asilikali lalikulu kwambiri komanso lamphamvu. Koma iye* sadzapambana chifukwa adzamukonzera chiwembu.

  • Danieli
    Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019
    • 11:25

      Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

      5/2020, ptsa. 4-5

      Nsanja ya Olonda,

      1/15/1999, ptsa. 30-31

      Ulosi wa Danieli, ptsa. 240-241

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena