Luka 8:49 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 49 Ali mkati molankhula, panafika nthumwi ya mtsogoleri wa sunagoge uja, ndipo anamuuza kuti: “Mwana wanu uja wamwalira. Musiyeni Mphunzitsiyu musamuvutitse.”+
49 Ali mkati molankhula, panafika nthumwi ya mtsogoleri wa sunagoge uja, ndipo anamuuza kuti: “Mwana wanu uja wamwalira. Musiyeni Mphunzitsiyu musamuvutitse.”+