Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 27:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Popeza dokolo silinali labwino kukhalapo nthawi yozizira, anthu ambiri anagwirizana ndi zoti achokepo. Iwo ankafuna kuona ngati nʼzotheka kukafika ku Finikesi kuti akakhale kumeneko nthawi yozizira. Finikesi linali doko la Kerete loyangʼana kumpoto chakumʼmawa ndi kumʼmwera chakumʼmawa.

  • Machitidwe
    Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019
    • 27:12

      Kuchitira Umboni Mokwanira, tsa. 207

      Nsanja ya Olonda,

      3/15/1999, tsa. 31

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena