Chivumbulutso 21:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Mzindawo sunafunikirenso kuwala kwa dzuwa kapena kwa mwezi, chifukwa kuwala kwa ulemerero wa Mulungu kunkaunikira mzindawo+ ndipo Mwanawankhosa ndi amene anali nyale yake.+ Chivumbulutso Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 21:23 Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 308-309
23 Mzindawo sunafunikirenso kuwala kwa dzuwa kapena kwa mwezi, chifukwa kuwala kwa ulemerero wa Mulungu kunkaunikira mzindawo+ ndipo Mwanawankhosa ndi amene anali nyale yake.+