Chivumbulutso 22:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Komanso, usiku sudzakhalakonso+ ndipo sadzafunikiranso kuwala kwa nyale kapena kwa dzuwa, chifukwa Yehova* Mulungu adzawaunikira.+ Ndipo iwo adzalamulira monga mafumu mpaka kalekale.+ Chivumbulutso Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 22:5 Nsanja ya Olonda,1/15/2012, tsa. 30 Mapeto a Chivumbulutso, tsa. 313
5 Komanso, usiku sudzakhalakonso+ ndipo sadzafunikiranso kuwala kwa nyale kapena kwa dzuwa, chifukwa Yehova* Mulungu adzawaunikira.+ Ndipo iwo adzalamulira monga mafumu mpaka kalekale.+