Genesis 31:40 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 40 Ndinkangokhalira kutenthedwa ndi dzuwa usana ndi kuzizidwa ndi mphepo usiku, ndipo tulo sindinkationa.+
40 Ndinkangokhalira kutenthedwa ndi dzuwa usana ndi kuzizidwa ndi mphepo usiku, ndipo tulo sindinkationa.+