-
Ekisodo 1:19Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
19 Poyankha azambawo anauza Farao kuti: “Amayi achiheberi sali ngati amayi achiiguputo. Popeza amayi achiheberi ndi amphamvu, mzamba asanafike iwo amakhala atabereka kale.”
-