18 “Uza Aroni ndi ana ake ndi ana onse a Isiraeli kuti, ‘Mwamuna aliyense wa nyumba ya Isiraeli, kapena mlendo wokhala mu Isiraeli amene akupereka nsembe+ pofuna kukwaniritsa lonjezo lake lililonse,+ kapena amene akupereka nsembe yake yaufulu,+ imene akuipereka kwa Yehova monga nsembe yopsereza,