1 Mafumu 17:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 “Nyamuka, upite ku Zarefati+ m’dziko la Sidoni ukakhale kumeneko. Ine ndikalamula mayi wina wa kumeneko, mkazi wamasiye, kuti azikakupatsa chakudya.” 1 Mafumu Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 17:9 Nsanja ya Olonda,2/15/2014, ptsa. 13-144/1/1992, ptsa. 18-19
9 “Nyamuka, upite ku Zarefati+ m’dziko la Sidoni ukakhale kumeneko. Ine ndikalamula mayi wina wa kumeneko, mkazi wamasiye, kuti azikakupatsa chakudya.”