-
2 Mbiri 23:18Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
18 Kuwonjezera apo, Yehoyada anapereka ntchito za panyumba ya Yehova kwa ansembe ndi Alevi amene Davide+ anawaika m’magulu panyumba ya Yehova, kuti azipereka nsembe zopsereza za Yehova mogwirizana ndi zimene zinalembedwa m’chilamulo cha Mose.+ Anawauza kuti azizipereka mosangalala poimba nyimbo motsatira ndondomeko imene Davide anakhazikitsa.
-