-
2 Mbiri 24:6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
6 Ndiyeno mfumuyo inaitana mtsogoleri wawo Yehoyada n’kumufunsa kuti:+ “Bwanji simunafunse Alevi kuti afotokoze za nkhani yobweretsa msonkho wopatulika kuchokera kwa anthu a ku Yuda ndi Yerusalemu? Si paja anayenera kubweretsa msonkho umene Mose+ mtumiki wa Yehova analamula, msonkho wopatulika wa mpingo wa Isiraeli wogwiritsa ntchito pachihema cha Umboni?+
-