-
Mlaliki 9:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Zimene zimachitikira anthu onse n’zofanana.+ Pali mapeto amodzi+ kwa munthu wolungama+ ndi woipa,+ kwa munthu wabwino, woyera, ndi wodetsedwa, ndiponso kwa munthu amene amapereka nsembe ndi amene sapereka nsembe. Munthu wabwino n’chimodzimodzi ndi munthu wochimwa.+ Munthu amene amalumbira mosaganizira bwino n’chimodzimodzi ndi amene amaopa kulumbira.+
-