Danieli 7:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 “Pambuyo pa zimenezi, ndinaona chilombo china chooneka ngati kambuku*+ koma chinali ndi mapiko anayi a mbalame pamsana pake. Chilombochi chinali ndi mitu inayi+ ndipo chinapatsidwa ulamuliro. Danieli Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 7:6 Nsanja ya Olonda,6/15/2012, ptsa. 10-114/15/1988, ptsa. 22-2410/1/1986, tsa. 7 Ulosi wa Danieli, ptsa. 134-135
6 “Pambuyo pa zimenezi, ndinaona chilombo china chooneka ngati kambuku*+ koma chinali ndi mapiko anayi a mbalame pamsana pake. Chilombochi chinali ndi mitu inayi+ ndipo chinapatsidwa ulamuliro.
7:6 Nsanja ya Olonda,6/15/2012, ptsa. 10-114/15/1988, ptsa. 22-2410/1/1986, tsa. 7 Ulosi wa Danieli, ptsa. 134-135