-
Danieli 7:19Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
19 “Ndiyeno ndinali ndi chidwi chofuna kudziwa zambiri zokhudza chilombo chachinayi chija, chimene chinali chosiyana ndi zina zonse. Chilombo chimenechi chinali choopsa kwambiri. Mano ake anali achitsulo, zikhadabo zake zinali zamkuwa, ndipo chinali kudya zinthu ndi kuziphwanyaphwanya. Zotsala chinali kuzipondaponda ndi mapazi ake.+
-