Mateyu 21:33 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 33 “Mverani fanizo lina: Panali munthu wina yemwe analima munda wa mpesa+ ndi kumanga mpanda kuzungulira mundawo. Komanso anakumba dzenje loponderamo mphesa ndi kumanga nsanja.+ Atatero anausiya m’manja mwa alimi n’kupita kudziko lina.+ Mateyu Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 21:33 Yesu—Ndi Njira, tsa. 246 Nsanja ya Olonda,1/1/1990, tsa. 8
33 “Mverani fanizo lina: Panali munthu wina yemwe analima munda wa mpesa+ ndi kumanga mpanda kuzungulira mundawo. Komanso anakumba dzenje loponderamo mphesa ndi kumanga nsanja.+ Atatero anausiya m’manja mwa alimi n’kupita kudziko lina.+