-
Luka 2:36Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
36 Kunalinso Anna mneneri wamkazi, mwana wa Fanueli, wa fuko la Aseri. Mayi ameneyu anali wachikulire kwambiri, ndipo anakhala ndi mwamuna wake zaka 7 zokha kuchokera pa unamwali wake.
-
-
1. Kuwala Kwenikweni kwa DzikoMalifalensi a Mavidiyo a Uthenga Wabwino wa Yesu
-
-
Anna analankhula zokhudza mwanayo (gnj 1 48:52–50:21)
-