-
Machitidwe 5:21Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
21 Atamva zimenezi, analowa m’kachisi m’mawa kwambiri ndi kuyamba kuphunzitsa.
Koma mkulu wa ansembe ndi onse amene anali naye atafika, anasonkhanitsa pamodzi Khoti Lalikulu la Ayuda ndi bungwe lonse la akulu a ana a Isiraeli.+ Pamenepo anatumiza alonda kundende kuja kuti akatenge atumwiwo ndi kubwera nawo.
-