-
Aroma 15:16Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
16 Ndinapatsidwa kukoma mtima kumeneku kuti ndigwire ntchito yolengeza uthenga wabwino wa Mulungu monga wantchito wa Khristu Yesu, wotumikira anthu a mitundu ina.+ Cholinga changa pogwira ntchito yopatulikayi+ n’chakuti mitundu ina ya anthu iperekedwe+ kwa Mulungu ngati mphatso yovomerezeka+ imene yayeretsedwa ndi mzimu woyera.+
-