3 Ndikupempha iwenso wantchito mnzanga weniweni,+ kuti upitirize kuwathandiza amayi amenewa. Iwo ayesetsa limodzi ndi ine pa ntchito+ ya uthenga wabwino. Achita zimenezi limodzinso ndi Kilementi ndi antchito anzanga ena onse,+ amene mayina awo+ ali m’buku la moyo.+